1 Samuel 31:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma anthu a ku Yabesi-Giliyadi atamva zimene Afilisti adaamchita Saulo,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma pamene a ku Yabesi-Giliyadi anamva zimene Afilisti anamchitira Saulo,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene anthu a ku Yabesi Giliyadi anamva zimene Afilisti anachitira Sauli,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma pamene a ku Jabezi Gileadi anamva zimene Afilisti anamcitira Sauli,