1 Samuel 8:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adamuuza kuti, “Taonani, inu tsopanotu mwakhwima, ndipo ana anu sali ndi makhalidwe onga anu. Tsono mutipatse mfumu kuti izitilamulira, monga m'mene ikuchitira mitundu ina ya anthu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nanena naye, Taonani, mwakalamba, ndipo ana anu satsanza makhalidwe anu; tsono, mutilongere mfumu kuti ikatiweruze, monga umo muchitidwa m'mitundu yonse ya anthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anati kwa iye “Taonani, inu mwakula tsopano ndipo ana anu sakutsata makhalidwe anu abwino. Tsono mutipatse mfumu kuti izitilamulira, monga momwe ikuchitira mitundu ina yonseyi.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
nanena naye, Taonani, mwakalamba, ndipo ana anu satsanza makhalidwe anu; tsono, mutilongere mfumu kuti ikatiweruze, monga umo mucitidwa m'mitundu yonse ya anthu.