1 Samuel 8:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero tsono umvere zimene iwowo akunena. Koma ndiye uŵachenjeze kwambiri, ndipo uŵauzitse za mkhalidwe wake wa mfumu imene izidzaŵalamulirayo.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake tsono umvere mau ao; koma uwachenjeze kolimba, ndi kuwadziwitsa makhalidwe ake a mfumu imene idzawaweruza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono amvere zimene akunena, koma uwachenjeze kwambiri ndipo uwawuzitse za khalidwe la mfumu imene idzawalamulire.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace tsono umvere mau ao koma uwacenjeze kolimba, ndi kuwadziwitsa makhalidwe ace a mfumu imene idzawaweruza.