1 Thessalonians 2:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu ndinu mboni, Mulungu yemwe ndi mboninso, kuti mkhalidwe wathu pakati pa inu okhulupirira unali wangwiro, wolungama, ndi wopanda cholakwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Inu ndinu mboni, Mulungunso, kuti tinakhala oyera mtima ndi olungama ndi osalakwa kwa inu akukhulupirira;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu ndinu mboni, ndiponso Mulungu, kuti tinali oyera mtima, olungama ndi wopanda chifukwa pakati panu amene munakhulupirira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Inu ndinu mboni, Mulungunso, kuti tinakhala oyera mtima ndi olungama ndi osalakwa kwa inu akukhulupirira;