1 Thessalonians 2:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nchifukwa chake tidaayesetsa kubweranso kwanuko. Ineyo Paulo, ndidaayesa kangapo, koma Satana adaatilepheretsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
chifukwa tinafuna kudza kwa inu, inedi Paulo ndatero kamodzi kapena kawiri; koma Satana anatiletsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti ife tinafuna kubweranso kwa inu, makamaka ine Paulo, ndinayesa kangapo koma Satana anatiletsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
cifukwa tinafuna kudza kwa inu, inedi Paulo ndatero kamodzi kapena kawiri; koma Satana anatiletsa.