1 Thessalonians 3:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tikupempha kuti Mulungu Atate athu mwini, ndi Ambuye athu Yesu atikonzere njira yabwino kuti tidzafike kwanuko.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma Mulungu Atate wathu mwini yekha, ndi Ambuye wathu Yesu atitsogolere m'njira yakufika kwa inu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tikupempha kuti Mulungu ndi Atate athu mwini, ndi Ambuye athu Yesu, atikonzere njira yabwino kuti tidzafike kwanuko.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma Mulungu Atate wathu mwini yekha, ndi Ambuye wathu Yesu atitsogolere m'njira yakufika kwa inu;