1 Thessalonians 4:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
kuti akunja azikulemekezani, ndi kuti inuyo mukhale osadalira wina aliyense.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti mukayende oona mtima pa iwo a kunja, ndi kukhala osasowa kanthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mukatero akunja adzalemekeza makhalidwe anu a tsiku ndi tsiku, ndi kuti inuyo mukhale osadalira wina aliyense.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
kuti mukayende oona mtima pa iwo a kunja, ndi kukhala osasowa kanthu.