1 Thessalonians 5:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
koma zonse muziziyesa bwino, kuti muwonetsetse ngati nzoona. Musunge zimene zili zabwino,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yesani zonse; sungani chokomacho,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesani zinthu zonse. Gwiritsitsani chimene ndi chabwino.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yesani zonse; sungani cokomaco,