1 Timothy 2:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kwenikweni adzikongoletse ndi ntchito zabwino, monga ayenera kuchitira akazi amene amati ndi opembedza Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
komatu (umo mokomera akazi akuvomereza kulemekeza Mulungu), mwa ntchito zabwino.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma adzikongoletse ndi ntchito zabwino zoyenera mayi wopembedza Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
komatu (umo mokomera akazi akubvomereza kulemekeza Mulungu), mwa nchito zabwino.