1 Timothy 2:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sindilola kuti mkazi aziphunzitsa kapena kukhala ndi ulamuliro pa amuna. Mkazi kwake nkukhala chete.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma sindilola ine kuti mkazi aphunzitse, kapena kulamulira mwamuna; komatu akhale chete.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine sindikulola kuti amayi aziphunzitsa kapena kulamulira amuna; koma akhale chete.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma sindilola ine kuti mkazi aphunzitse, kapena kulamulira mwamuna; komatu akhale cete.