1 Timothy 3:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Asakhale munthu wolandiridwa mu mpingo chatsopano, kuwopa kuti angadzitukumule nkulangidwa monga momwe Satana adalangidwira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Asakhale wophunza, kuti podzitukumula ungamgwere mlandu wa mdierekezi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Asakhale wongotembenuka mtima kumene kuopa kuti angadzitukumule napezeka pa chilango monga Satana.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Asakhale wophunza, kuti podzitukumula ungamgwere mlandu wa mdierekezi.