1 Timothy 4:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ntchito zimenezi uzizichita mosamala ndi modzipereka, kuti anthu onse aone kuti moyo wako wautumiki ukukulirakulira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Izi uzisamalitse; mu izi ukhale; kuti kukula mtima kwako kuonekere kwa onse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Uzichita zimenezi mosamalitsa ndi modzipereka kwathunthu, kuti aliyense aone kuti ukupita mʼtsogolo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Izi uzisamalitse; mu izi ukhale; kuti kukula mtima kwako kuonekere kwa onse.