1 Timothy 4:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngati abale uŵalangiza zimenezi, udzakhala mtumiki wabwino wa Khristu Yesu, woleredwa ndi mau a chikhulupiriro ndi a chiphunzitso choona chimene wakhala ukutsata.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati ukumbutsa abale zinthu izi, udzakhala mtumiki wabwino wa Khristu Yesu, woleredwa m'mauwo a chikhulupiriro, ndi malangizo abwino amene udawatsata;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati abale uwalangiza zimenezi, udzakhala mtumiki wabwino wa Khristu Yesu, woleredwa mʼchoonadi cha chikhulupiriro ndi mʼchiphunzitso chabwino chimene wakhala ukutsata.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati ukumbutsa abale zinthu izi, udzakhala mtumiki wabwino wa Kristu Yesu, woleredwa m'mauwo a cikhulupiriro, ndi malangizo abwino amene udawatsata;