1 Timothy 5:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wachikulire usamdzudzule mokalipa, koma umchenjeze monga ngati bambo wako. Amuna achinyamata uzikhalitsana nawo ngati abale ako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mkulu usamdzudzule, komatu umdandaulire ngati atate; anyamata ngati abale;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usadzudzule munthu wachikulire mokalipa, koma umuchenjeze ngati abambo ako. Achinyamata uwatenge ngati abale ako.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mkulu usamdzudzule, komatu umdandaulire ngati atate; anyamata ngati abale;