2 Chronicles 11:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Chauta adadza kwa Semaya, m'meneri wake, namlamula kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma mau a Yehova anadza kwa Semaya munthu wa Mulunguyo, ndi kuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Yehova anayankhula ndi munthu wa Mulungu Semaya kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma mau a Yehova anadza kwa Semaya munthu wa Mulunguyo, ndi kuti,