2 Chronicles 14:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Asa adanyamuka kuti akakomane naye, ndipo onsewo adandanditsa magulu ao ankhondo ku chigwa cha Zefati ku Maresa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Natuluka Asa pamaso pake, nanika nkhondoyi m'chigwa cha Zefati ku Maresa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Asa anapita kukakumana naye ndipo anakhala pa mizere yawo ya nkhondo mʼchigwa cha Zefata pafupi ndi Maresa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Naturuka Asa pamaso pace, nanika nkhondoyi m'cigwa ca Sefata ku Maresa.