2 Chronicles 14:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero Chauta adagonjetsa anthu a ku Etiopiya pamaso pa Asa ndi pa anthu a ku Yuda, ndipo anthu a ku Etiopiyawo adathaŵa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yehova anakantha Akusi pamaso pa Asa ndi Yuda, nathawa Akusi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova anakantha Akusi pamaso pa Asa ndi Ayuda. Akusi anathawa,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehova anakantha Akusi pamaso pa Asa ndi Yuda, nathawa Akusi.