2 Chronicles 14:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo adagwetsa makola a ziŵeto, ndi kutenga nkhosa zochuluka, pamodzi ndi ngamira. Kenaka adabwerera ku Yerusalemu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anakanthanso a m'mahema a ng'ombe, nalanda nkhosa zochuluka, ndi ngamira; nabwerera kunka ku Yerusalemu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anakathiranso nkhondo misasa ya anthu oweta ziweto ndipo anatenga nkhosa zambiri, mbuzi ndi ngamira. Atatero anabwerera ku Yerusalemu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anakanthanso a m'mahema a ng'ombe, nalanda nkhosa zocuruka, ndi ngamila; nabwerera kumka ku Yerusalemu.