2 Chronicles 15:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mzimu wa Mulungu udamtsikira Azariya mwana wa Odedi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo mzimu wa Mulungu unagwera Azariya mwana wa Odedi,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mzimu wa Mulungu unabwera pa Azariya mwana wa Odedi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo mzimu wa Mulungu unagwera Azariya mwana wa Odedi,