2 Chronicles 15:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono panalibenso nkhondo mpaka chaka cha 35 cha ufumu wa Asa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo panalibenso nkhondo mpaka Asa atakhala mfumu zaka makumi atatu mphambu zinai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Panalibenso nkhondo mpaka chaka cha 35 cha ufumu wa Asa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo panalibenso nkhondo mpaka Asa atakhala mfumu zaka makumi atatu mphambu zinai.