2 Chronicles 17:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ku Benjamini, Eliyada munthu wolimba mtima, anali ndi anthu 200,000 amauta ndi azishango.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi a Benjamini: Eliyada ngwazi yamphamvu, ndi pamodzi ndi iye zikwi mazana awiri ogwira mauta ndi zikopa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuchokera ku Benjamini: Eliada, msilikali wolimba mtima, anali ndi anthu 200,000 amene anali ndi mauta ndi zishango;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi a Benjamini: Eliyada ngwazi yamphamvu, ndi pamodzi ndi iye zikwi mazana awiri ogwira mauta ndi zikopa;