2 Chronicles 21:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono adalandira kalata kwa mneneri Eliya, yonena kuti, “Chauta, Mulungu wa Davide, kholo lanu, akunena kuti, ‘Sudatsate chitsanzo cha Yehosafati bambo wako, kapenanso cha Asa, mfumu ya ku Yuda,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anamdzera kalata wofuma kwa Eliya mneneri, ndi kuti, Atero Yehova Mulungu wa Davide atate wanu, Popeza simunayenda m'njira za Yehosafati atate wanu, kapena m'njira za Asa mfumu ya Yuda,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehoramu analandira kalata yochokera kwa mneneri Eliya yonena kuti, “Yehova Mulungu wa Davide abambo ako akuti, ‘Iwe sunayende mʼnjira ya Yehosafati abambo ako kapena Asa mfumu ya Yuda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anamdzera kalata wofuma kwa Eliya mneneri, ndi kuti, Atero Yehova Mulungu wa Davide atate wanu, Popeza simunayenda m'njira za Yehosafati atate wanu, kapena m'njira za Asa mfumu ya Yuda,