2 Chronicles 22:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwanayo adakhala ndi iwowo zaka zisanu ndi chimodzi, akubisala m'Nyumba ya Chauta, pamene Ataliya ankalamulira dzikolo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo iye anali nao wobisika m'nyumba ya Mulungu zaka zisanu ndi chimodzi; nakhala Ataliya mfumu yaikazi ya dziko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwanayo anakhala mobisala pamodzi ndi iwo mu Nyumba ya Mulungu kwa zaka zisanu ndi chimodzi muulamuliro wa Ataliya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo iye anali nao wobisika m'nyumba ya Mulungu zaka zisanu ndi cimodzi; nakhala Ataliya mfumu yaikazi ya dziko.