2 Chronicles 22:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iyeyonso ankatsata chitsanzo cha banja la Ahabu, poti mai wake ndiye ankamupatsa uphungu woipa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iyenso anayenda m'njira za nyumba ya Ahabu; pakuti wompangira ndi make achite choipa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nayenso anayenda mʼnjira ya banja la Ahabu, pakuti amayi ake anamulimbikitsa kuchita zolakwika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iyenso anayenda m'njira za nyumba ya Ahabu; pakuti wompangira ndi mace acite coipa,