2 Chronicles 23:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Ataliya atamva phokoso la anthu othamangira komweko akutamanda mfumu, adapita ku Nyumba ya Chauta kukaŵapeza anthuwo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pamene Ataliya anamva phokoso la anthu alikuthamanga ndi kulemekeza mfumu, anadza kwa anthu m'nyumba ya Yehova;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ataliya atamva phokoso la anthu akuthamanga ndi kukondwerera mfumu, anapita ku Nyumba ya Yehova komwe kunali anthuko.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pamene Ataliya anamva phokoso la anthu alikuthamanga ndi kulemekeza mfumu, anadza kwa anthu m'nyumba ya Yehova;