2 Chronicles 23:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Yehoyada adachititsa chipangano pakati pa iye mwini, ndi anthu onse ndi mfumunso, kuti iwowo akhale anthu akeake a Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yehoyada anachita pangano pakati pa iye, ndi anthu onse, ndi mfumu, kuti adzakhala anthu a Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono Yehoyada anachita pangano, iye mwini ndi anthu onse ndiponso mfumu kuti adzakhala anthu a Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehoyada anacita pangano pakati pa iye, ndi anthu onse, ndi mfumu, kuti adzakhala anthu a Yehova.