2 Chronicles 24:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja anthu ake a Ataliya, mkazi woipa uja, adaaonongapo Nyumba ya Mulungu, ndiponso adaatenga zinthu zonse zopatulika za ku Nyumba ya Chautayo, nazipereka kwa Abaala.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti ana a Ataliya mkazi woipa uja anathyola chitseko cha nyumba ya Mulungu, natenga zopatulidwa zonse za nyumba ya Yehova kuzipereka kwa Baala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ana a mkazi woyipa, Ataliya, anathyola chitseko cha Nyumba ya Mulungu ndipo anagwiritsa ntchito zinthu zopatulika popembedza Baala.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti ana a Ataliya mkazi woipa uja anathyola citseko ca nyumba ya Mulungu, natenga zopatulidwa zonse za nyumba ya Yehova kuzipereka kwa Baala.