2 Chronicles 28:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja Aedomu anali atathiranso nkhondo ku Yuda, ndipo adaagonjetsa Yudayo, natenga anthu kuti akhale akapolo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Aedomu anadzanso, nakantha Yuda, natenga andende.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ankhondo a ku Edomu anabweranso ndi kuthira nkhondo Yuda ndi kugwira akapolo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Aedomu anadzanso, nakantha Yuda, natenga andende.