2 Chronicles 29:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwowo adasonkhanitsa abale ao, ndipo adadziyeretsa, naloŵa m'Nyumba ya Chauta kuti aiyeretse monga momwe mfumu idaalamulira, potsata mau a Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anamemeza abale ao, nadzipatula, nalowa monga adawauza mfumu mwa mau a Yehova, kuyeretsa nyumba ya Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atasonkhanitsa abale awo ndi kudziyeretsa, iwo anapita kukayeretsa Nyumba ya Yehova, monga inalamulira mfumu, potsatira mawu a Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anamemeza abale ao, nadzipatula, nalowa monga adawauza mfumu mwa mau a Yehova, kuyeretsa nyumba ya Yehova.