2 Chronicles 3:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Solomoniyo adayamba kumanga pa mwezi wachiŵiri wa chaka chachinai cha ufumu wake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nayamba kumanga tsiku lachiwiri la mwezi wachiwiri, chaka chachinai cha ufumu wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anayamba kumanga pa tsiku lachiwiri la mwezi wachiwiri mʼchaka chachinayi cha ulamuliro wake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nayamba kumanga tsiku laciwiri la mwezi waciwiri, caka cacinai ca ufumu wace.