2 Chronicles 33:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta adalankhula ndi Manase ndiponso ndi anthu ake, koma iwo sadasamaleko.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yehova analankhula ndi Manase ndi anthu ake, koma sanasamalire.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova anayankhula kwa Manase ndi anthu ake, koma iwo sanasamaleko.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehova analankhula ndi Manase ndi anthu ace, koma sanasamalira.