2 Chronicles 33:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono anyamata ake adamchita chiwembu, namupha m'nyumba mwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anyamata ake anampangira chiwembu, namupha m'nyumba yakeyake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Akuluakulu a Amoni anamuchita chiwembu ndipo anamupha mʼnyumba yake yaufumu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anyamata ace anampangira ciwembu, namupha m'nyumba yace yace.