2 Chronicles 33:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adamanga maguwa m'mabwalo aŵiri a Nyumba ya Chauta, kumangira zolengedwa zonse zamumlengalenga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Namangiranso khamu lonse la kuthambo maguwa a nsembe m'mabwalo awiri a nyumba ya Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mʼmabwalo onse awiri a Nyumba ya Yehova anamangamo maguwa ansembe a zolengedwa zonse zamlengalenga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Namangiranso khamu lonse la kuthambo maguwa a nsembe m'mabwalo awiri a nyumba ya Yehoya.