2 Chronicles 34:29 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo mfumu idatumiza mau kukaitana akuluakulu onse a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu kuti adzasonkhane.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo mfumu inatumiza anthu, nisonkhanitsa akuluakulu onse a Yuda ndi Yerusalemu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo mfumu inasonkhanitsa pamodzi akuluakulu onse a Yuda ndi Yerusalemu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo mfumu inatumiza anthu, nisonkhanitsa akulu akulu onse a Yuda ndi Yerusalemu.