2 Chronicles 36:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu am'dzikomo adatenga Yehowahazi mwana wa Yosiya, namlonga ufumu m'malo mwa atate ake ku Yerusalemu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo anthu a m'dziko anatenga Yehowahazi mwana wa Yosiya, namlonga ufumu m'Yerusalemu, m'malo mwa atate wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono anthu a mʼdzikomo anatenga Yehowahazi mwana wa Yosiya namuyika kukhala mfumu mu Yerusalemu mʼmalo mwa abambo ake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo anthu a m'dziko anatenga Yehoahazi mwana wa Yosiya, namlonga ufumu m'Yerusalemu, m'malo mwa atate wace.