2 Chronicles 36:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yehowahazi anali wa zaka 23 pamene ankaloŵa ufumu. Ndipo adalamulira miyezi itatu ku Yerusalemu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehowahazi anali wa zaka makumi awiri mphambu zitatu polowa ufumu wake, nakhala mfumu m'Yerusalemu miyezi itatu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yowahazi anali wa zaka 23 pamene anakhala mfumu ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa miyezi itatu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehoahazi anali wa zaka makumi awiri mphambu zitatu polowa ufumu wace, nakhala mfumu m'Yerusalemu miyezi itatu.