2 Chronicles 36:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yehoyakini anali wa zaka 18 pamene adaloŵa ufumu, ndipo adalamulira miyezi itatu ndi masiku khumi ku Yerusalemu. Iyeyo ankachita zoipa pamaso pa Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehoyakini anali wa zaka zisanu ndi zitatu polowa ufumu wake, nakhala mfumu m'Yerusalemu miyezi itatu, ndi masiku khumi; nachita choipa pamaso pa Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehoyakini anali ndi zaka 21 pamene anakhala mfumu ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa miyezi itatu ndi masiku khumi. Iye anachita zoyipa pamaso pa Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehoyakini anali wa zaka zisanu ndi zitatu polowa ufumu wace, nakhala mfumu m'Yerusalemu miyezi itatu, ndi masiku khumi; nacita coipa pamaso pa Yehova.