2 Chronicles 7:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Koma inu mukapatuka ndi kusiya malamulo anga ndi malangizo anga amene ndidakupatsani, mukamatumikira milungu ina ndi kumaipembedza,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma mukabwerera inu, ndi kusiya malemba anga, ndi malamulo anga, amene ndaika pamaso panu, ndi kumuka ndi kutumikira milungu ina ndi kuilambira;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Koma ngati iwe udzapatuka ndi kutaya malangizo ndi malamulo amene ndakupatsa ndi kupita kukatumikira milungu ina ndi kuyipembedza,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma mukabwerera inu, ndi kusiya malemba anga, ndi malamulo anga, amene ndaika pamaso panu, ndi kumuka ndi kutumikira milungu yina ndi kuilambira;