2 Corinthians 1:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pali Mulungu woona, ndikulumbira kuti mau athu amene timakuuzani sali “Inde” ndiponso “Ai”.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma Mulungu ali wokhulupirika, kuti mau athu a kwa inu sanakhala eya ndi iai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma zoona monga Mulungu ali wokhulupirika, uthenga wathu kwa inu siwakuti, “Inde” nʼkutinso “Ayi.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma Mulungu ali wokhulupirika, kuti mau athu a kwa inu sanakhala eya ndi iai.