2 Corinthians 10:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja Malembo akuti, “Wofuna kunyada, anyadire Ambuye.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma iye wodzitamandira adzitamandire mwa Ambuye;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma, “Ngati munthu akufuna kunyadira, anyadire mwa Ambuye.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma iye wodzitamandira adzitamandire mwa Ambuye;