2 Corinthians 10:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono musayese kuti ndikungokuwopsezani ndi makalata anga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti ndisaoneke monga ngati kukuopsani mwa akalatawo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine sindikufuna kuoneka ngati ndikukuopsezani ndi makalata anga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
kuti ndisaoneke monga ngati kukuopsani mwa akalatawo.