2 Corinthians 11:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono popeza kuti ambiri akunyadira zapansipano, inenso ndidzatero.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Popeza ambiri adzitamandira monga mwa thupi, inenso ndidzadzitamandira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Popeza ambiri akudzitama monga dziko lapansi limachitira, inenso ndidzitamanso.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Popeza ambiri adzitamandira monga mwa thupi, inenso ndidzadzitamandira.