2 Corinthians 11:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu mumati ndinu anzeru kwambiri, nchifukwa chake anthu opusa mumangoŵalekerera mokondwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti mulolana nao opanda nzeru mokondwera, pokhala anzeru inu nokha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu mumalolera kukhala ndi zitsiru mokondwera chifukwa mumati ndinu anzeru!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti mulolana nao opanda nzeru mokondwera, pokhala anzeru inu nokha.