2 Corinthians 11:23 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi iwo ndi atumiki a Khristu? Ndikulankhula ngati wamisala, ndine mtumiki woposa iwowo. Ndidagwira ntchito kwambiri kopambana iwo, kaŵirikaŵiri ndinali pafupi kufa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi ali atumiki a Khristu? (Ndilankhula monga moyaluka), makamaka ine; m'zivutinso mochulukira, m'ndende mochulukira, m'mikwingwirima mosawerengeka, muimfa kawirikawiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi iwo ndi atumiki a Khristu? Ndikuyankhula ngati wamisala. Ine ndine woposa iwowo. Ndagwira ntchito kwambiri kupambana iwo, ndakhala ndikuyikidwa mʼndende kawirikawiri, ndakwapulidwapo kwambiri, kawirikawiri ndinali pafupi kufa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi ali atumiki a Kristu? (ndilankhula monga moyaruka), makamaka ine; m'zibvutitso mocurukira, m'ndende mocurukira, m'mikwingwirima mosawerengeka, muimfa kawiri kawiri.