2 Corinthians 2:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Cholinga chake nkuti Satana asatichenjerere, paja tikudziŵa njira zake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti asatichenjerere Satana; pakuti sitikhala osadziwa machenjerero ake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kupewa kuti Satana angapezere mpata pa ife, pajatu timadziwa machenjerero ake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
kuti asaticenierere Satana; pakuti sitikhala osadziwa macenjerero ace.