2 Corinthians 2:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zoonadi tili ngati fungo labwino la Khristu lokomera Mulungu, pakati pa anthu amene akupulumuka ndi amene akutayika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti ife ndife fungo labwino la Khristu, kwa Mulungu, mwa iwo akupulumutsidwa, ndi mwa iwo akuonongeka; kwa ena fungo la imfa kuimfa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti kwa Mulungu ndife fungo labwino la Khristu pakati pa iwo amene akupulumutsidwa ndi amene akuwonongeka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti ife ndife pfungo labwino la Kristu, kwa Mulungu, mwa iwo akupulumutsidwa, ndi mwa iwo akuonongeka; kwa ena pfungo la imfa kuimfa;