2 Corinthians 2:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kwa amene akutayika, fungoli ndi la imfa, ndipo limaŵapha. Koma kwa amene akupulumuka, fungoli ndi la moyo, ndipo limaŵapatsa moyo. Nanga ndani angaithe ntchito yotere?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
koma kwa ena fungo la moyo kumoyo. Ndipo azikwanira ndani izi?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kwa amene akuwonongeka ndife fungo la imfa, limawapha. Ndipo kwa amene akupulumuka ndife fungo lamoyo, limawapatsa moyo. Ndani angayithe ntchito yotereyi?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
koma kwa ena pfungo la moyo kumoyo. Ndipo azikwanira ndani izi?