2 Corinthians 3:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Popeza kuti timayembekeza zimenezi, timalimba mtima kwambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pokhala nacho tsono chiyembekezo chotere, tilankhula ndi kukhazikika mtima kwakukulu,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho, popeza tili ndi chiyembekezo chotere, ndife olimba mtima kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pokhala naco tsono ciyembekezo cotere, tilankhula ndi kukhazikika mtima kwakukuru,