2 Corinthians 4:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma ngakhale Uthenga Wabwino umene timalalika uli wophimbika, ngwophimbika kwa okhawo amene akutayika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ngatinso Uthenga Wabwino wathu uphimbika, uphimbika mwa iwo akutayika;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ngakhale uthenga wathu wabwino utakhala wophimbika, ndi wophimbika kwa okhawo amene akutayika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ngatinso Uthenga Wabwino wathu uphimbika, uphimbika mwa iwo akutayika;