2 Corinthians 6:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono popeza kuti ndife ogwirizana ndi Mulungu pa ntchito yake, takupembani musaŵasandutse achabe madalitso amene Mulungu adakupatsani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ochita naye pamodzi tidandauliranso kuti musalandire chisomo cha Mulungu kwachabe inu,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pogwira naye ntchito pamodzi, tikukudandaulirani kuti musangolandira chisomo cha Mulungu pachabe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo a ocita naye pamodzi tidandauliranso kuti musalandire cisomo ca Mulungu kwacabe inu,